Search

ΔΩΡΕΑΝ ΤΥΠΩΜΕΝΑ ΒΙΒΛΙΑ,
eBOOKS ΚΑΙ ΒΙΒΛΙΑ ΗΧΟΥ

Το Ευαγγέλιο του Ύδατος και του Πνεύματος

Γκα 53

NZERU YA UTHENGA WABWINO WAKALE

Rev. Paul C. Jong | ISBN 9788928240777 | Σελίδες 422

Κατεβάστε ηλεκτρονικά βιβλία και ηχητικά βιβλία ΔΩΡΕΑΝ

Επιλέξτε την προτιμώμενη μορφή αρχείου και κατεβάστε με ασφάλεια στην κινητή συσκευή, τον υπολογιστή ή το tablet σας για να διαβάσετε και να ακούσετε τις συλλογές κηρυγμάτων οποιαδήποτε στιγμή και οπουδήποτε. Όλα τα ηλεκτρονικά βιβλία και ηχητικά βιβλία είναι εντελώς δωρεάν.

Μπορείτε να ακούσετε το ηχητικό βιβλίο μέσω του προγράμματος αναπαραγωγής παρακάτω. 🔻
Αποκτήστε ένα χαρτόδετο βιβλίο
Αγοράστε ένα χαρτόδετο βιβλίο στο Amazon
Zamkatimu

Mawu Oyamba 

1. Kodi Tchimo Loyamba la Anthu Ndi Chiani? (Marko 7:20-23) 
2. Kodi Uthenga Wabwino Unakwaniritsidwa ndi Mwazi Okha, kapena ndi Madzi, kapena ndi Zonse? (Eksodo 12:43-49) 
3. Ubwenzi Pakati Pa Utumiki Wa Yohane Mbatizi Ndi Uthenga Wabwino Wa Chitetezero Cha Machimo (Mateyu 21:32) 
4. Kodi Tanthauzo Leni Leni La kubadwanso Mwatsopano Ndi Chiani? (Yohane 3:1-15) 
5. Nsembe Yonsinthidwa (Ahebri 7:1-28)
6. Mwanawankhosa wa Mulungu Amene Achotsa Tchimo Lache La dziko Lapansi! (Yohane 1:29) 
7. Uthenga Wabwino Wa Chitetezero Omwe Wafufuta Machimo Anu Onse a Masiku Onse (Yohane 13:1-17)
8. Uthenga Wabwino Wakale Omwe Ungagonjetse Machimo a Dziko Lapansi (1 Yohane 5:4-9) 
 
Uthenga Wabwino wakale otchulidwa m’buku ili ndi Uthenga Wabwino oyamba otchedwa kuti “Uthenga Wabwino wa madzi ndi Mzimu.” Mpaka pano, komabe, Akristu ambiri sakudziwa kuti Uthenga Wabwino wa madzi ndi Mzimu ndiye Uthenga Wabwino oyamba, ndipo zotsatira zake akhulupilira molakwika mu ‘Uthenga wa hafu’. Ndi chifukwa chake chikhulupiliro chao sichipita patali, ndipo zakhala zosatheka kwa iwo kuona kukula mu uzimu. Chikhulupiliro chao chakhala choperewera nthawi zonse, chodzadza ndi malamulo kapena chikhulupiliro cha zinsinsi. Zotsatira zake sangadzithandize okha koma kukhala ndi mitima yochimwa. Kodi ndi mphamvu yanji ya uzimu yomwe Akristu otere angakhale nayo pamene adakali ndi machimo m’mitima yao? Chifukwa akhala Akristu opanda mphamvu, myoyo yao mu dziko lino ilibenso ntchito. Tinganene tsopano kuti Akristu alero ali ndi Uthenga wa hafu kuyambira pa nthawi yomwe mpingo oyamba unatha. Motero, tonse a ife tiyenera kuzindikiranso Uthenga Wabwino wakale tsopano nthawi isanathe, dziwani chikondi cha Mulungu choonadi ndi kukhulupilira mu chikondi choonadichi.
Περισσότερα

Βιβλία που σχετίζονται με αυτόν τον τίτλο

The New Life Mission

Συμμετάσχετε στην έρευνά μας

Πώς μάθατε για εμάς;