Search

ΔΩΡΕΑΝ ΤΥΠΩΜΕΝΑ ΒΙΒΛΙΑ,
eBOOKS ΚΑΙ ΒΙΒΛΙΑ ΗΧΟΥ

Το Ευαγγέλιο του Ύδατος και του Πνεύματος

Γκα-Ινδονησιακά 1

[Chichewa-Indonesia] KODI MWABADWADI MWATSOPANO MWA MADZI NDI MZIMU WOYERA? [Kusindikiza Kokonzedwanso Kwatsopano]-SUDAHKAH ANDA BENAR-BENAR DILAHIRKAN KEMBALI DARI AIR DAN ROH? [Edisi Revisi Baru]

Rev. Paul C. Jong | ISBN 9788928227358 | Σελίδες 941

Κατεβάστε ηλεκτρονικά βιβλία και ηχητικά βιβλία ΔΩΡΕΑΝ

Επιλέξτε την προτιμώμενη μορφή αρχείου και κατεβάστε με ασφάλεια στην κινητή συσκευή, τον υπολογιστή ή το tablet σας για να διαβάσετε και να ακούσετε τις συλλογές κηρυγμάτων οποιαδήποτε στιγμή και οπουδήποτε. Όλα τα ηλεκτρονικά βιβλία και ηχητικά βιβλία είναι εντελώς δωρεάν.

Μπορείτε να ακούσετε το ηχητικό βιβλίο μέσω του προγράμματος αναπαραγωγής παρακάτω. 🔻
Αποκτήστε ένα χαρτόδετο βιβλίο
Αγοράστε ένα χαρτόδετο βιβλίο στο Amazon
ZAM’KATIMU
 
Chigawo Choyamba — Maulaliki 
1. Choyamba Ife Tiyenera Kudziwa Machimo Athu kuti Tiomboledwe (Marko 7:8-9, 20-23)
2. Anthu Amabadwa Wochimwa (Marko 7:20-23)
3. Ngati Ife Tichita Zinthu Motsatira Lamulo, Kodi Ilo Lingatipulutse Ife? (Luka 10:25-30) 
4. Chiombolo cha Muyaya (Yohane 8:1-12) 
5. Ubatizo wa Yesu ndi Chitetezero cha Machimo (Mateyu 3:13-17)
6. Yesu Kristu Adadza mwa Madzi, Mwazi, ndi Mzimu Woyera (1 Yohane 5:1-12)
7. Ubatizo wa Yesu Ndi Chifaniziro cha Chipulumutso cha Ochimwa (1 Petro 3:20-22)
8. Uthenga Wabwino wa Chiombolo Chochuluka (Yohane 13:1-17)
 
Chigawo Chachiwiri — Mau Owonjezera
1. Kufotokoza Kowonjezera
2. Mafunso ndi Mayankho
 
(Chichewa)
Mutu waukulu wa bukuli ndi "kubadwa mwatsopano mwa Madzi ndi Mzimu Woyera." Ili ndi chiyambi chake pa mutuwu. Mwanjira ina, bukuli limatiwuza momveka bwino chomwe kubadwa mwatsopano kuli ndi mmene tingabadwire mwatsopano mwa madzi ndi Mzimu Woyera molingana ndi Baibulo. Madzi amaimira ubatizo wa Yesu ku Yordano ndipo Baibulo limati machimo athu onse anaperekedwa kwa Yesu pamene Iye anabatizidwa ndi Yohane Mbatizi. Yohane anali woimira anthu onse ndiponso mdzukulu wa Aroni, Wansembe Wamkulu. Aroni anasanjika manja ake pamutu pa mbuzi yopereka nsembe ndipo anapititsira machimo onse a chaka cha Aisraeli pa iyo pa Tsiku la Chiyanjanitso. Ichi ndi chithunzithunzi cha zinthu zabwino zikubwera. Ubatizo wa Yesu ndi chifaniziro cha kusanjika manja. Yesu anabatizidwa m`njira ya kusanjika manja ku Yordano. Choncho Iye anachotsa machimo onse a dziko lapansi kudzera mu ubatizo Wake ndipo anapachikidwa kuti alipire machimowo. Koma Akhristu ambiri sadziwa chifukwa chake Yesu anabatizidwa ndi Yohane Mbatizi mu Yordano. Ubatizo wa Yesu ndi mawu ofunika kwambiri a bukuli ndiponso gawo losatheka kuchotsa la Uthenga Wabwino wa Madzi ndi Mzimu Woyera. Tikhoza kubadwa mwatsopano pokhapokha titakhulupirira mu ubatizo wa Yesu ndi Mtanda Wake.
 
(Indonesian)
Subjek utama dari judul ini adalah "dilahirkan kembali dari Air dan Roh." Ini memiliki keaslian dalam subjek tersebut. Dengan kata lain, buku ini dengan jelas memberitahu kita apa arti dilahirkan kembali dan bagaimana dilahirkan kembali dari Air dan Roh sesuai dengan Alkitab. Air melambangkan baptisan Yesus di sungai Yordan dan Alkitab mengatakan bahwa semua dosa kita dipindahkan kepada Yesus ketika Dia dibaptis oleh Yohanes Pembaptis. Yohanes adalah wakil dari seluruh umat manusia dan keturunan Imam Besar Harun. Harun meletakkan tangannya di atas kepala Azazel dan memindahkan semua dosa tahunan orang Israel ke atasnya pada Hari Pendamaian. Itu adalah bayangan dari hal-hal baik yang akan datang. Baptisan Yesus adalah simbol dari penumpangan tangan.
Yesus dibaptis dalam bentuk penumpangan tangan di sungai Yordan. Jadi Dia menanggung segala dosa dunia melalui baptisan-Nya dan disalibkan untuk membayar dosa-dosa itu. Tetapi kebanyakan orang Kristen tidak tahu mengapa Yesus dibaptis oleh Yohanes Pembaptis di sungai Yordan. Baptisan Yesus adalah kata kunci dari buku ini, dan bagian yang tak terpisahkan dari Injil Air dan Roh. Kita bisa dilahirkan kembali hanya dengan percaya kepada baptisan Yesus dan Salib-Nya.
 
 Next 
Chichewa 2: BWELERANI KU UTHENGA WABWINO WA MADZI NDI MZIMU
BWELERANI KU UTHENGA WABWINO WA MADZI NDI MZIMU
 
Indonesian 2: KEMBALI KEPADA INJIL AIR DAN ROH
KEMBALI KEPADA INJIL AIR DAN ROH
Περισσότερα

Βιβλία που σχετίζονται με αυτόν τον τίτλο

The New Life Mission

Συμμετάσχετε στην έρευνά μας

Πώς μάθατε για εμάς;