Search

LIBROS IMPRESOS,
ELECTRÓNICOS Y EN AUDIO GRATIS

El Tabernáculo

Chichewa 9

CHIHEMA: Chithunzi Chatsatanetsatane cha Yesu Kristu ( I )

Rev. Paul C. Jong | ISBN 9788928231843 | Páginas 378

Descargue eBooks y audiolibros GRATIS

Elija su formato de archivo preferido y descárguelo de forma segura en su dispositivo móvil, PC o tableta para leer y escuchar las colecciones de sermones en cualquier momento y lugar. Todos los eBooks y audiolibros son completamente gratuitos.

Puede escuchar el audiolibro a través del reproductor de abajo. 🔻
Tenga un libro en rústica
Compre un libro en rústica en Amazon
ZAMKATIMU
 
Mau Oyamba 

1. Chipulumutso cha Ochimwa Choonetsedwa mu Chihema (Eksodo 27:9-21) 
2. Ambuye Wathu Yemwe Anabvutika Chifukwa cha Ife (Yesaya 52:13-53:9) 
3. Yawe Mulungu Wamoyo (Eksodo 34:1-8) 
4. Chifukwa Chimene Mulungu Anaitanira Mose ku Phiri la Sinai (Eksodo 19:1-6) 
5. M’mene Aisrayeli Ankaperekera Nsembe mu Chihema: Mbiri Yoyamba (Genesis 15:1-21) 
6. Lonjezo La Mulungu Lokhazikitsidwa mu Pangano Lake la Mdulidwe Lidakali ndi Ntchito kwa Ife (Genesis 17:1-14) 
7. Zipangizo Zomangira Chihema Zomwe Zinaika Maziko a Chikhulupiliro (Eksodo 25:1-9) 
8. Mtundu wa Chipata cha Bwalo la Chihema (Eksodo 27:9-19) 
9. Chikhulupiliro Choonetsedwa mu Guwa la Nsembe (Exodus 27:1-8) 
10. Chikhulupiliro Choonetsedwa mu Mkhate Wosambiramo (Eksodo 30:17-21) 
11. Umboni wa Chipulumutso 
 
Kodi tingapedze motani coonadi co bitsala mu Cihema? Ndi pokhapo podzindikira uthenga wa madzi ndi Mzimu, ceni ceni ca Cihema, ndi pamene tingadziwe yankho ku funso limeneli.
Mcoonadi, nsaru zomwe zitaonekedwa pa kohomo la bwalo la Cihema limatisonyedza zincito za Yesu Kristu mu Cipangano ca Tsopano cimene cidapulumutsa anthu amudziko la pansi. Munjira yotere, Mau a mu Cipangano ca Kale ya mu Cihema ndi Mau a mu Cipangano ca Tsopano yali cimodzimodzi yo fanana, monga nsaru za mu Cihema. Koma, mwatsoka, ici coonadi cankhala cobitsika kwa nthgawi yaitali kwa iwo amene amafuna funa coonadi mu Ukristu.
Pobwera padziko lino, Yesu Kristu anabatizidwa ndi Yohane ndipo ana ketsa mwadzi Wace pa Mtanda. Kopanda kumvetsetsa ndi kukhulupirira mu uthenga wa madzi ndi Mzimu, palibe Umodzi waife yemwe anga dziwe coonadi cobvumbulutsidwa mu Cihema. Tiyenera kudziwa tsopano coonadi ici ca Chihema ndi kukhulupiriramo. Tonsefe tiyenera kudziwa ndi kukhulupirira mu coonadi coonekedwa nsaru zimene zitayalidwa pabwalo ya pakhomo ya Cihema.
Más
Reproductor de audiolibros

Libros relacionados con este título

The New Life Mission

Participe en nuestra encuesta

¿Cómo se enteró de nosotros?