Search

無料の本、電子ブック、
オーディオブック

水と御霊の福音

チェワ語-インドネシア語 1

[Chichewa-Indonesia] KODI MWABADWADI MWATSOPANO MWA MADZI NDI MZIMU WOYERA? [Kusindikiza Kokonzedwanso Kwatsopano]-SUDAHKAH ANDA BENAR-BENAR DILAHIRKAN KEMBALI DARI AIR DAN ROH? [Edisi Revisi Baru]

Rev. Paul C. Jong | ISBN 9788928227358 | ページ 941

電子書籍とオーディオブックを無料でダウンロード

お好みのファイル形式を選択し、モバイル端末、PC、タブレットに安全にダウンロードして、説教集をいつでもどこでも読んだり聴いたりすることができます。すべての電子書籍とオーディオブックは完全無料です。

下記のプレーヤーでオーディオブックを聴くことができます。🔻
ペーパーバックを所有
Amazonでペーパーバックを購入
ZAM’KATIMU
 
Chigawo Choyamba — Maulaliki 
1. Choyamba Ife Tiyenera Kudziwa Machimo Athu kuti Tiomboledwe (Marko 7:8-9, 20-23)
2. Anthu Amabadwa Wochimwa (Marko 7:20-23)
3. Ngati Ife Tichita Zinthu Motsatira Lamulo, Kodi Ilo Lingatipulutse Ife? (Luka 10:25-30) 
4. Chiombolo cha Muyaya (Yohane 8:1-12) 
5. Ubatizo wa Yesu ndi Chitetezero cha Machimo (Mateyu 3:13-17)
6. Yesu Kristu Adadza mwa Madzi, Mwazi, ndi Mzimu Woyera (1 Yohane 5:1-12)
7. Ubatizo wa Yesu Ndi Chifaniziro cha Chipulumutso cha Ochimwa (1 Petro 3:20-22)
8. Uthenga Wabwino wa Chiombolo Chochuluka (Yohane 13:1-17)
 
Chigawo Chachiwiri — Mau Owonjezera
1. Kufotokoza Kowonjezera
2. Mafunso ndi Mayankho
 
(Chichewa)
Mutu waukulu wa bukuli ndi "kubadwa mwatsopano mwa Madzi ndi Mzimu Woyera." Ili ndi chiyambi chake pa mutuwu. Mwanjira ina, bukuli limatiwuza momveka bwino chomwe kubadwa mwatsopano kuli ndi mmene tingabadwire mwatsopano mwa madzi ndi Mzimu Woyera molingana ndi Baibulo. Madzi amaimira ubatizo wa Yesu ku Yordano ndipo Baibulo limati machimo athu onse anaperekedwa kwa Yesu pamene Iye anabatizidwa ndi Yohane Mbatizi. Yohane anali woimira anthu onse ndiponso mdzukulu wa Aroni, Wansembe Wamkulu. Aroni anasanjika manja ake pamutu pa mbuzi yopereka nsembe ndipo anapititsira machimo onse a chaka cha Aisraeli pa iyo pa Tsiku la Chiyanjanitso. Ichi ndi chithunzithunzi cha zinthu zabwino zikubwera. Ubatizo wa Yesu ndi chifaniziro cha kusanjika manja. Yesu anabatizidwa m`njira ya kusanjika manja ku Yordano. Choncho Iye anachotsa machimo onse a dziko lapansi kudzera mu ubatizo Wake ndipo anapachikidwa kuti alipire machimowo. Koma Akhristu ambiri sadziwa chifukwa chake Yesu anabatizidwa ndi Yohane Mbatizi mu Yordano. Ubatizo wa Yesu ndi mawu ofunika kwambiri a bukuli ndiponso gawo losatheka kuchotsa la Uthenga Wabwino wa Madzi ndi Mzimu Woyera. Tikhoza kubadwa mwatsopano pokhapokha titakhulupirira mu ubatizo wa Yesu ndi Mtanda Wake.
 
(Indonesian)
Subjek utama dari judul ini adalah "dilahirkan kembali dari Air dan Roh." Ini memiliki keaslian dalam subjek tersebut. Dengan kata lain, buku ini dengan jelas memberitahu kita apa arti dilahirkan kembali dan bagaimana dilahirkan kembali dari Air dan Roh sesuai dengan Alkitab. Air melambangkan baptisan Yesus di sungai Yordan dan Alkitab mengatakan bahwa semua dosa kita dipindahkan kepada Yesus ketika Dia dibaptis oleh Yohanes Pembaptis. Yohanes adalah wakil dari seluruh umat manusia dan keturunan Imam Besar Harun. Harun meletakkan tangannya di atas kepala Azazel dan memindahkan semua dosa tahunan orang Israel ke atasnya pada Hari Pendamaian. Itu adalah bayangan dari hal-hal baik yang akan datang. Baptisan Yesus adalah simbol dari penumpangan tangan.
Yesus dibaptis dalam bentuk penumpangan tangan di sungai Yordan. Jadi Dia menanggung segala dosa dunia melalui baptisan-Nya dan disalibkan untuk membayar dosa-dosa itu. Tetapi kebanyakan orang Kristen tidak tahu mengapa Yesus dibaptis oleh Yohanes Pembaptis di sungai Yordan. Baptisan Yesus adalah kata kunci dari buku ini, dan bagian yang tak terpisahkan dari Injil Air dan Roh. Kita bisa dilahirkan kembali hanya dengan percaya kepada baptisan Yesus dan Salib-Nya.
 
 Next 
Chichewa 2: BWELERANI KU UTHENGA WABWINO WA MADZI NDI MZIMU
BWELERANI KU UTHENGA WABWINO WA MADZI NDI MZIMU
 
Indonesian 2: KEMBALI KEPADA INJIL AIR DAN ROH
KEMBALI KEPADA INJIL AIR DAN ROH
もっと見る

このタイトルに関連する書籍

The New Life Mission

アンケートに答える

当サイトをどのようにお知りになりましたか?