Search

免費電子書和有聲讀物

水與靈的福音

奇切瓦語-德語 1

[Chichewa-Deutsch] KODI MWABADWADI MWATSOPANO MWA MADZI NDI MZIMU WOYERA? [Kusindikiza Kokonzedwanso Kwatsopano]-SIND SIE WIRKLICH AUS WASSER UND GEIST VON NEUEM GEBOREN WORDEN? [Neue überarbeitete Auflage]

Rev. Paul C. Jong | ISBN 9788928227686 | 頁碼 935

下載免費電子書和有聲讀物

選擇您喜歡的文件格式,安全下載到手機、電腦或平板電腦,隨時隨地閱讀和收聽講道集。所有電子書和有聲讀物都完全免費。

您可以通過下方播放器收聽有聲讀物。🔻
擁有平裝書
在亞馬遜購買平裝書
ZAM’KATIMU
 
Chigawo Choyamba — Maulaliki 
1. Choyamba Ife Tiyenera Kudziwa Machimo Athu kuti Tiomboledwe (Marko 7:8-9, 20-23)
2. Anthu Amabadwa Wochimwa (Marko 7:20-23)
3. Ngati Ife Tichita Zinthu Motsatira Lamulo, Kodi Ilo Lingatipulutse Ife? (Luka 10:25-30) 
4. Chiombolo cha Muyaya (Yohane 8:1-12) 
5. Ubatizo wa Yesu ndi Chitetezero cha Machimo (Mateyu 3:13-17)
6. Yesu Kristu Adadza mwa Madzi, Mwazi, ndi Mzimu Woyera (1 Yohane 5:1-12)
7. Ubatizo wa Yesu Ndi Chifaniziro cha Chipulumutso cha Ochimwa (1 Petro 3:20-22)
8. Uthenga Wabwino wa Chiombolo Chochuluka (Yohane 13:1-17)
 
Chigawo Chachiwiri — Mau Owonjezera
1. Kufotokoza Kowonjezera
2. Mafunso ndi Mayankho
 
(Chichewa)
Mutu waukulu wa bukuli ndi "kubadwa mwatsopano mwa Madzi ndi Mzimu Woyera." Ili ndi chiyambi chake pa mutuwu. Mwanjira ina, bukuli limatiwuza momveka bwino chomwe kubadwa mwatsopano kuli ndi mmene tingabadwire mwatsopano mwa madzi ndi Mzimu Woyera molingana ndi Baibulo. Madzi amaimira ubatizo wa Yesu ku Yordano ndipo Baibulo limati machimo athu onse anaperekedwa kwa Yesu pamene Iye anabatizidwa ndi Yohane Mbatizi. Yohane anali woimira anthu onse ndiponso mdzukulu wa Aroni, Wansembe Wamkulu. Aroni anasanjika manja ake pamutu pa mbuzi yopereka nsembe ndipo anapititsira machimo onse a chaka cha Aisraeli pa iyo pa Tsiku la Chiyanjanitso. Ichi ndi chithunzithunzi cha zinthu zabwino zikubwera. Ubatizo wa Yesu ndi chifaniziro cha kusanjika manja. Yesu anabatizidwa m`njira ya kusanjika manja ku Yordano. Choncho Iye anachotsa machimo onse a dziko lapansi kudzera mu ubatizo Wake ndipo anapachikidwa kuti alipire machimowo. Koma Akhristu ambiri sadziwa chifukwa chake Yesu anabatizidwa ndi Yohane Mbatizi mu Yordano. Ubatizo wa Yesu ndi mawu ofunika kwambiri a bukuli ndiponso gawo losatheka kuchotsa la Uthenga Wabwino wa Madzi ndi Mzimu Woyera. Tikhoza kubadwa mwatsopano pokhapokha titakhulupirira mu ubatizo wa Yesu ndi Mtanda Wake.
 
(German)
Das Hauptthema dieses Titels ist "aus Wasser und Geist von neuem geboren zu werden." Er hat die Orginalität zu diesem Thema. Mit anderen Worten, dieses Buch sagt und deutlich, was es bedeutet, wiedergeboren zu werden und wie man aus Wasser und Geist in strikter Übereinstimmung mit der Bibel wiedergeboren wird. Das Wasser symbolisiert die Taufe Jesu im Jordan und die Bibel sagt, dass alle unsere Sünden an Jesus weitergegeben wurden, als Er von Johannes dem Täufer getauft wurde. Johannes war der Vertreter der gesamten Menschheit und ein Nachkomme von Aaron dem Hohepriester. Aaron legte seine Hände auf den Kopf des Sündenbocks und gab alle jährlichen Sünden der Israeliten am Versöhnungstag an ihn weiter. Es ist ein Schatten von den zukünftigen Gütern. Die Taufe Jesu ist das Gegenbild des Auflegens von Händen.
Jesus wurde in Form des Auflegens von Händen im Jordan getauft. Also nahm Er alle Sünden der Welt durch Seine Taufe weg und wurde gekreuzigt, um für die Sünden zu bezahlen. Aber die meisten Christen wissen nicht, warum Jesus im Jordan von Johannes dem Täufer getauft wurde. Jesus Taufe ist das Schlüsselwort dieses Buches und der unverzichtbare Teil des Evangeliums des Wassers und des Geistes. Wir können nur von neuem geboren werden, wenn wir an die Taufe Jesu und Sein Kreuz glauben.
 
 Next 
Chichewa 2: BWELERANI KU UTHENGA WABWINO WA MADZI NDI MZIMU
BWELERANI KU UTHENGA WABWINO WA MADZI NDI MZIMU
 
German 2: Rückkehr zum Evangelium des Wassers und des Geistes
Rückkehr zum Evangelium des Wassers und des Geistes
更多

與該標題相關的書籍

The New Life Mission

參加我們的調查

您是如何得知我們的?