Search

免費電子書和有聲讀物

水與靈的福音

奇切瓦語-烏克蘭語 1

[Chichewa-Українська] KODI MWABADWADI MWATSOPANO MWA MADZI NDI MZIMU WOYERA? [Kusindikiza Kokonzedwanso Kwatsopano]-ЧИ ВИ СПРАВДІ НАРОДИЛИСЯ ЗНОВУ ВІД ВОДИ ТА ДУХА? [Нове перероблене видання]

Rev. Paul C. Jong | ISBN 9788928225248 | 頁碼 931

下載免費電子書和有聲讀物

選擇您喜歡的文件格式,安全下載到手機、電腦或平板電腦,隨時隨地閱讀和收聽講道集。所有電子書和有聲讀物都完全免費。

您可以通過下方播放器收聽有聲讀物。🔻
擁有平裝書
在亞馬遜購買平裝書
ZAM’KATIMU
 
Chigawo Choyamba — Maulaliki 
1. Choyamba Ife Tiyenera Kudziwa Machimo Athu kuti Tiomboledwe (Marko 7:8-9, 20-23)
2. Anthu Amabadwa Wochimwa (Marko 7:20-23)
3. Ngati Ife Tichita Zinthu Motsatira Lamulo, Kodi Ilo Lingatipulutse Ife? (Luka 10:25-30) 
4. Chiombolo cha Muyaya (Yohane 8:1-12) 
5. Ubatizo wa Yesu ndi Chitetezero cha Machimo (Mateyu 3:13-17)
6. Yesu Kristu Adadza mwa Madzi, Mwazi, ndi Mzimu Woyera (1 Yohane 5:1-12)
7. Ubatizo wa Yesu Ndi Chifaniziro cha Chipulumutso cha Ochimwa (1 Petro 3:20-22)
8. Uthenga Wabwino wa Chiombolo Chochuluka (Yohane 13:1-17)
 
Chigawo Chachiwiri — Mau Owonjezera
1. Kufotokoza Kowonjezera
2. Mafunso ndi Mayankho
 
(Chichewa)
Mutu waukulu wa bukuli ndi "kubadwa mwatsopano mwa Madzi ndi Mzimu Woyera." Ili ndi chiyambi chake pa mutuwu. Mwanjira ina, bukuli limatiwuza momveka bwino chomwe kubadwa mwatsopano kuli ndi mmene tingabadwire mwatsopano mwa madzi ndi Mzimu Woyera molingana ndi Baibulo. Madzi amaimira ubatizo wa Yesu ku Yordano ndipo Baibulo limati machimo athu onse anaperekedwa kwa Yesu pamene Iye anabatizidwa ndi Yohane Mbatizi. Yohane anali woimira anthu onse ndiponso mdzukulu wa Aroni, Wansembe Wamkulu. Aroni anasanjika manja ake pamutu pa mbuzi yopereka nsembe ndipo anapititsira machimo onse a chaka cha Aisraeli pa iyo pa Tsiku la Chiyanjanitso. Ichi ndi chithunzithunzi cha zinthu zabwino zikubwera. Ubatizo wa Yesu ndi chifaniziro cha kusanjika manja. Yesu anabatizidwa m`njira ya kusanjika manja ku Yordano. Choncho Iye anachotsa machimo onse a dziko lapansi kudzera mu ubatizo Wake ndipo anapachikidwa kuti alipire machimowo. Koma Akhristu ambiri sadziwa chifukwa chake Yesu anabatizidwa ndi Yohane Mbatizi mu Yordano. Ubatizo wa Yesu ndi mawu ofunika kwambiri a bukuli ndiponso gawo losatheka kuchotsa la Uthenga Wabwino wa Madzi ndi Mzimu Woyera. Tikhoza kubadwa mwatsopano pokhapokha titakhulupirira mu ubatizo wa Yesu ndi Mtanda Wake.
 
(Ukrainian)
Основна тема цієї книги - "народитися знову з води та Духа". Вона оригінально висвітлює це питання. Іншими словами, ця книга чітко розповідає нам, що таке народження знову і як народитися знову з води та Духа у чіткій відповідності з Біблією. Вода символізує хрещення Ісуса в Йордані, і Біблія говорить, що всі наші гріхи були передані Ісусу, коли Його охрестив Іван Хреститель. Іван був представником всього людства і нащадком Аарона Первосвященника. Аарон клав руки на голову козла відпущення і передавав йому всі річні гріхи ізраїльтян у День Спокути. Це тінь майбутнього добра. Хрещення Ісуса є прообразом покладання рук.
Ісус прийняв хрещення у вигляді покладання рук на Йордані. Тож Він забрав усі гріхи світу Своїм хрещенням і був розп’ятий, щоб заплатити за гріхи. Але більшість християн не знають, чому Іван Хреститель охрестив Ісуса в Йордані. Хрещення Ісуса є ключовим словом цієї книги та невід’ємною частиною євангелія води та Духа. Ми можемо народитися знову, лише якщо віримо в хрещення Ісуса та Його Хрест.
 
 Next 
Chichewa 2: BWELERANI KU UTHENGA WABWINO WA MADZI NDI MZIMU
BWELERANI KU UTHENGA WABWINO WA MADZI NDI MZIMU
 
Ukrainian 2: Повернення до Євангелія Води та Духа
Повернення до Євангелія Води та Духа
更多

與該標題相關的書籍

The New Life Mission

參加我們的調查

您是如何得知我們的?