Search

免費印刷書籍、
電子書和有聲讀物

水與靈的福音

奇切瓦語-印尼語 1

[Chichewa-Indonesia] KODI MWABADWADI MWATSOPANO MWA MADZI NDI MZIMU WOYERA? [Kusindikiza Kokonzedwanso Kwatsopano]-SUDAHKAH ANDA BENAR-BENAR DILAHIRKAN KEMBALI DARI AIR DAN ROH? [Edisi Revisi Baru]

Rev. Paul C. Jong | ISBN 9788928227358 | 頁碼 941

下載免費電子書和有聲讀物

選擇您喜歡的文件格式,安全下載到手機、電腦或平板電腦,隨時隨地閱讀和收聽講道集。所有電子書和有聲讀物都完全免費。

您可以通過下方播放器收聽有聲讀物。🔻
擁有平裝書
在亞馬遜購買平裝書
ZAM’KATIMU
 
Chigawo Choyamba — Maulaliki 
1. Choyamba Ife Tiyenera Kudziwa Machimo Athu kuti Tiomboledwe (Marko 7:8-9, 20-23)
2. Anthu Amabadwa Wochimwa (Marko 7:20-23)
3. Ngati Ife Tichita Zinthu Motsatira Lamulo, Kodi Ilo Lingatipulutse Ife? (Luka 10:25-30) 
4. Chiombolo cha Muyaya (Yohane 8:1-12) 
5. Ubatizo wa Yesu ndi Chitetezero cha Machimo (Mateyu 3:13-17)
6. Yesu Kristu Adadza mwa Madzi, Mwazi, ndi Mzimu Woyera (1 Yohane 5:1-12)
7. Ubatizo wa Yesu Ndi Chifaniziro cha Chipulumutso cha Ochimwa (1 Petro 3:20-22)
8. Uthenga Wabwino wa Chiombolo Chochuluka (Yohane 13:1-17)
 
Chigawo Chachiwiri — Mau Owonjezera
1. Kufotokoza Kowonjezera
2. Mafunso ndi Mayankho
 
(Chichewa)
Mutu waukulu wa bukuli ndi "kubadwa mwatsopano mwa Madzi ndi Mzimu Woyera." Ili ndi chiyambi chake pa mutuwu. Mwanjira ina, bukuli limatiwuza momveka bwino chomwe kubadwa mwatsopano kuli ndi mmene tingabadwire mwatsopano mwa madzi ndi Mzimu Woyera molingana ndi Baibulo. Madzi amaimira ubatizo wa Yesu ku Yordano ndipo Baibulo limati machimo athu onse anaperekedwa kwa Yesu pamene Iye anabatizidwa ndi Yohane Mbatizi. Yohane anali woimira anthu onse ndiponso mdzukulu wa Aroni, Wansembe Wamkulu. Aroni anasanjika manja ake pamutu pa mbuzi yopereka nsembe ndipo anapititsira machimo onse a chaka cha Aisraeli pa iyo pa Tsiku la Chiyanjanitso. Ichi ndi chithunzithunzi cha zinthu zabwino zikubwera. Ubatizo wa Yesu ndi chifaniziro cha kusanjika manja. Yesu anabatizidwa m`njira ya kusanjika manja ku Yordano. Choncho Iye anachotsa machimo onse a dziko lapansi kudzera mu ubatizo Wake ndipo anapachikidwa kuti alipire machimowo. Koma Akhristu ambiri sadziwa chifukwa chake Yesu anabatizidwa ndi Yohane Mbatizi mu Yordano. Ubatizo wa Yesu ndi mawu ofunika kwambiri a bukuli ndiponso gawo losatheka kuchotsa la Uthenga Wabwino wa Madzi ndi Mzimu Woyera. Tikhoza kubadwa mwatsopano pokhapokha titakhulupirira mu ubatizo wa Yesu ndi Mtanda Wake.
 
(Indonesian)
Subjek utama dari judul ini adalah "dilahirkan kembali dari Air dan Roh." Ini memiliki keaslian dalam subjek tersebut. Dengan kata lain, buku ini dengan jelas memberitahu kita apa arti dilahirkan kembali dan bagaimana dilahirkan kembali dari Air dan Roh sesuai dengan Alkitab. Air melambangkan baptisan Yesus di sungai Yordan dan Alkitab mengatakan bahwa semua dosa kita dipindahkan kepada Yesus ketika Dia dibaptis oleh Yohanes Pembaptis. Yohanes adalah wakil dari seluruh umat manusia dan keturunan Imam Besar Harun. Harun meletakkan tangannya di atas kepala Azazel dan memindahkan semua dosa tahunan orang Israel ke atasnya pada Hari Pendamaian. Itu adalah bayangan dari hal-hal baik yang akan datang. Baptisan Yesus adalah simbol dari penumpangan tangan.
Yesus dibaptis dalam bentuk penumpangan tangan di sungai Yordan. Jadi Dia menanggung segala dosa dunia melalui baptisan-Nya dan disalibkan untuk membayar dosa-dosa itu. Tetapi kebanyakan orang Kristen tidak tahu mengapa Yesus dibaptis oleh Yohanes Pembaptis di sungai Yordan. Baptisan Yesus adalah kata kunci dari buku ini, dan bagian yang tak terpisahkan dari Injil Air dan Roh. Kita bisa dilahirkan kembali hanya dengan percaya kepada baptisan Yesus dan Salib-Nya.
 
 Next 
Chichewa 2: BWELERANI KU UTHENGA WABWINO WA MADZI NDI MZIMU
BWELERANI KU UTHENGA WABWINO WA MADZI NDI MZIMU
 
Indonesian 2: KEMBALI KEPADA INJIL AIR DAN ROH
KEMBALI KEPADA INJIL AIR DAN ROH
更多

與該標題相關的書籍

The New Life Mission

參加我們的調查

您是如何得知我們的?