Search

SÁCH IN,
SÁCH ĐIỆN TỬ VÀ SÁCH NÓI MIỄN PHÍ

Phúc-âm của Nước và Thánh Linh

Chichewa 53

NZERU YA UTHENGA WABWINO WAKALE

Rev. Paul C. Jong | ISBN 9788928240777 | Trang 422

Tải xuống sách điện tử và sách nói MIỄN PHÍ

Chọn định dạng tệp ưa thích và tải xuống an toàn vào điện thoại di động, máy tính hoặc máy tính bảng để đọc và nghe các bộ sưu tập bài giảng mọi lúc mọi nơi. Tất cả sách điện tử và sách nói đều hoàn toàn miễn phí.

Bạn có thể nghe sách nói qua trình phát bên dưới. 🔻
Sở hữu sách in
Mua sách in trên Amazon
Zamkatimu

Mawu Oyamba 

1. Kodi Tchimo Loyamba la Anthu Ndi Chiani? (Marko 7:20-23) 
2. Kodi Uthenga Wabwino Unakwaniritsidwa ndi Mwazi Okha, kapena ndi Madzi, kapena ndi Zonse? (Eksodo 12:43-49) 
3. Ubwenzi Pakati Pa Utumiki Wa Yohane Mbatizi Ndi Uthenga Wabwino Wa Chitetezero Cha Machimo (Mateyu 21:32) 
4. Kodi Tanthauzo Leni Leni La kubadwanso Mwatsopano Ndi Chiani? (Yohane 3:1-15) 
5. Nsembe Yonsinthidwa (Ahebri 7:1-28)
6. Mwanawankhosa wa Mulungu Amene Achotsa Tchimo Lache La dziko Lapansi! (Yohane 1:29) 
7. Uthenga Wabwino Wa Chitetezero Omwe Wafufuta Machimo Anu Onse a Masiku Onse (Yohane 13:1-17)
8. Uthenga Wabwino Wakale Omwe Ungagonjetse Machimo a Dziko Lapansi (1 Yohane 5:4-9) 
 
Uthenga Wabwino wakale otchulidwa m’buku ili ndi Uthenga Wabwino oyamba otchedwa kuti “Uthenga Wabwino wa madzi ndi Mzimu.” Mpaka pano, komabe, Akristu ambiri sakudziwa kuti Uthenga Wabwino wa madzi ndi Mzimu ndiye Uthenga Wabwino oyamba, ndipo zotsatira zake akhulupilira molakwika mu ‘Uthenga wa hafu’. Ndi chifukwa chake chikhulupiliro chao sichipita patali, ndipo zakhala zosatheka kwa iwo kuona kukula mu uzimu. Chikhulupiliro chao chakhala choperewera nthawi zonse, chodzadza ndi malamulo kapena chikhulupiliro cha zinsinsi. Zotsatira zake sangadzithandize okha koma kukhala ndi mitima yochimwa. Kodi ndi mphamvu yanji ya uzimu yomwe Akristu otere angakhale nayo pamene adakali ndi machimo m’mitima yao? Chifukwa akhala Akristu opanda mphamvu, myoyo yao mu dziko lino ilibenso ntchito. Tinganene tsopano kuti Akristu alero ali ndi Uthenga wa hafu kuyambira pa nthawi yomwe mpingo oyamba unatha. Motero, tonse a ife tiyenera kuzindikiranso Uthenga Wabwino wakale tsopano nthawi isanathe, dziwani chikondi cha Mulungu choonadi ndi kukhulupilira mu chikondi choonadichi.
Thêm

Những sách liên quan đến tựa đề này

The New Life Mission

Tham gia khảo sát của chúng tôi

Bạn biết đến chúng tôi qua đâu?