Search

LIVRES NUMÉRIQUES ET LIVRES AUDIO GRATUITS

L’évangile de l’eau et de l’Esprit

Chichewa-Français 1

[Chichewa-Français] KODI MWABADWADI MWATSOPANO MWA MADZI NDI MZIMU WOYERA? [Kusindikiza Kokonzedwanso Kwatsopano]-ÊTES-VOUS VRAIMENT NÉ DE NOUVEAU D’EAU ET D’ESPRIT ? [Nouvelle Édition Révisée]

Rev. Paul C. Jong | ISBN 9788928227761 | Pages 921

Téléchargez des livres numériques et livres audio GRATUITS

Choisissez votre format de fichier préféré et téléchargez-le en toute sécurité sur votre appareil mobile, PC ou tablette pour lire et écouter les collections de sermons n'importe quand et n'importe où. Tous les livres numériques et livres audio sont entièrement gratuits.

Vous pouvez écouter le livre audio via le lecteur ci-dessous. 🔻
Possédez un livre broché
Téléchargement gratuit de livres audio
ZAM’KATIMU
 
Chigawo Choyamba — Maulaliki 
1. Choyamba Ife Tiyenera Kudziwa Machimo Athu kuti Tiomboledwe (Marko 7:8-9, 20-23)
2. Anthu Amabadwa Wochimwa (Marko 7:20-23)
3. Ngati Ife Tichita Zinthu Motsatira Lamulo, Kodi Ilo Lingatipulutse Ife? (Luka 10:25-30) 
4. Chiombolo cha Muyaya (Yohane 8:1-12) 
5. Ubatizo wa Yesu ndi Chitetezero cha Machimo (Mateyu 3:13-17)
6. Yesu Kristu Adadza mwa Madzi, Mwazi, ndi Mzimu Woyera (1 Yohane 5:1-12)
7. Ubatizo wa Yesu Ndi Chifaniziro cha Chipulumutso cha Ochimwa (1 Petro 3:20-22)
8. Uthenga Wabwino wa Chiombolo Chochuluka (Yohane 13:1-17)
 
Chigawo Chachiwiri — Mau Owonjezera
1. Kufotokoza Kowonjezera
2. Mafunso ndi Mayankho
 
(Chichewa)
Mutu waukulu wa bukuli ndi "kubadwa mwatsopano mwa Madzi ndi Mzimu Woyera." Ili ndi chiyambi chake pa mutuwu. Mwanjira ina, bukuli limatiwuza momveka bwino chomwe kubadwa mwatsopano kuli ndi mmene tingabadwire mwatsopano mwa madzi ndi Mzimu Woyera molingana ndi Baibulo. Madzi amaimira ubatizo wa Yesu ku Yordano ndipo Baibulo limati machimo athu onse anaperekedwa kwa Yesu pamene Iye anabatizidwa ndi Yohane Mbatizi. Yohane anali woimira anthu onse ndiponso mdzukulu wa Aroni, Wansembe Wamkulu. Aroni anasanjika manja ake pamutu pa mbuzi yopereka nsembe ndipo anapititsira machimo onse a chaka cha Aisraeli pa iyo pa Tsiku la Chiyanjanitso. Ichi ndi chithunzithunzi cha zinthu zabwino zikubwera. Ubatizo wa Yesu ndi chifaniziro cha kusanjika manja. Yesu anabatizidwa m`njira ya kusanjika manja ku Yordano. Choncho Iye anachotsa machimo onse a dziko lapansi kudzera mu ubatizo Wake ndipo anapachikidwa kuti alipire machimowo. Koma Akhristu ambiri sadziwa chifukwa chake Yesu anabatizidwa ndi Yohane Mbatizi mu Yordano. Ubatizo wa Yesu ndi mawu ofunika kwambiri a bukuli ndiponso gawo losatheka kuchotsa la Uthenga Wabwino wa Madzi ndi Mzimu Woyera. Tikhoza kubadwa mwatsopano pokhapokha titakhulupirira mu ubatizo wa Yesu ndi Mtanda Wake.
 
(French)
Le sujet principal de ce livre est « naître de nouveau de l’eau et de l’Esprit ». Il est original sur le sujet. En d’autres termes, ce livre nous dit clairement ce que signifie naître de nouveau et comment naître de nouveau de l’eau et de l’Esprit en stricte conformité avec la Bible. L’eau symbolise le baptême de Jésus au Jourdain et la Bible dit que tous nos péchés ont été transférés sur Jésus lorsqu’il a été baptisé par Jean-Baptiste. Jean était le représentant de toute l’humanité et un descendant d’Aaron, le grand prêtre. Aaron posa ses mains sur la tête du bouc émissaire et transféra sur elle tous les péchés annuels des Israélites le jour des expiations. C’est l’ombre des bonnes choses à venir. Le baptême de Jésus est l’antitype de l’imposition des mains. Jésus a été baptisé sous la forme de l’imposition des mains au Jourdain. Il a donc pris tous les péchés du monde par son baptême et a été crucifié pour payer pour les péchés. Mais la plupart des chrétiens ne savent pas pourquoi Jésus a été baptisé par Jean-Baptiste au Jourdain. Le baptême de Jésus est le mot-clé de ce livre et la partie indispensable de l’Évangile de l’eau et de l’Esprit. Nous ne pouvons naître de nouveau qu’en croyant au baptême de Jésus et à sa croix.
 
 Next 
Chichewa 2: BWELERANI KU UTHENGA WABWINO WA MADZI NDI MZIMU
BWELERANI KU UTHENGA WABWINO WA MADZI NDI MZIMU
 
French 2: RETOURNEZ À L’ÉVANGILE DE L’EAU ET DE L’ESPRIT
RETOURNEZ À L’ÉVANGILE DE L’EAU ET DE L’ESPRIT
Plus

Livres liés à ce titre

The New Life Mission

Participez à notre enquête

Comment avez-vous entendu parler de nous ?