Search

ספרים מודפסים,
ספרים אלקטרונים וספרי אודיו חינמיים

בשורת המים והרוח

סִינִית 65

KODI CHOFUNIKIRA NDI CHIANI KWA INU KUTI MUBADWENSO MWATSOPANO?

Rev. Paul C. Jong | ISBN 9788928240876 | עמודים 397

חינם הורד ספרים אלקטרוניים וספרי שמע

בחר את תבנית הקובץ המועדפת עליך והורד בבטחה למכשיר הנייד, המחשב או הטאבלט שלך כדי לקרוא ולהאזין לאוספי הדרשות בכל זמן ומקום. כל הספרים האלקטרוניים וספרי השמע ניתנים לחלוטין בחינם.

🔻ניתן להאזין לספר השמע באמצעות הנגן שלמטה.
היה בעלים של ספר בכריכה רכה
קנה ספר בכריכה רכה באמזון
Zamkatimu

Mawu Oyamba 
1. Kodi Ndindani Olambira Mumzimu Ndi M’coonadi? (Yohane 4:1-24) 
2. Kodi Zikutanthauza Chiani Kubadwadi Mwatsopano? (Yohane 4:1-19) 
3. Kanani Maganizo Anu (2 Mafumu 5:15-19)
4. Umunthu Wanu Weni Weni Ndi Chikondi Cha Ambuye (Yohane 3:16) 
5. Tiyenera Kubadwa Mwatsopano Pokhulupilira mu Uthenga Wabwino wa Madzi Ndi Mzimu (Yohane 3:1-5)
6. Chikhulupiliro Chomwe Chimagonjetsa Dziko Lino (Yohane 15:1-9) 
7. Kukhulupilira mu Ntchito Ya Mulungu Ndi Kugwira Ntchito Ya Mulungu (Yohane 6:16-29) 
8. Yesu Watsuka Mapazi athu Monga M’mene Anatsukira Mapazi a Petro (Yohane 13:1-11) 
9. Ambuye Wathu Watidalitsa Ife Kuti Titsate Iye Ngakhale Tiri Ndi Zolakwa Zambiri (Yohane 21:15-19)
10. Chofunikira Chenicheni Pogawana Chiyanjano Mwa Kristu (1 Yohane 1-10) 
11. Kodi Zikutanthauza Chiani Pamene Baibulo Lanena Kuti Yense Wakukhala Mwa Mulungu Sachimwa? (1 Yohane 3:1-10) 
12. Kodi Mukufunitsitsadi Kuti Chikhulupiliro Chanu Chikhale Chofanana Monga Chikhulupiliro Cha Petro? (Mateyu 16:13-20) 
13 Chilungamo Cha Ambuye Ndi Chofunika Kotheratu Kwa Ife Amene Timachita Tchimo Nthawi Zonse (Mateyu 9:9-13) 
 
Akristu lero ayenera kusintha maganizo ao. Iwo ayenera kukhulupilira mu Uthenga Wabwino wa madzi ndi Mzimu woperekedwa ndi Mulungu monga chipulumutso chao cheni cheni. Tonse tiyenera kuthokoza Ambuye potipatsa ife Uthenga umenewu Wabwino wa madzi ndi Mzimu. Kodi m’malo mwake tinganene bwanji kuti ntchito ya Ambuye ya chipulumutso yomwe yaombola ife ku machimo onse a dziko kuti ndiyolakwika? Kudzera m’bukuli pa Uthenga Wabwino wa madzi ndi Mzimu, ali yense tsopano ayenera kubadwa mwatsopano pokhulupilira muchipulumutso chomwe Ambuye wakwaniritsa kamodzi kokha. Ngati simukutsimikizabe za izi, muyenera kachiwiri kusinkhasinkha mwakuya pa chilungamo cha Mulungu chomwe Ambuye wapereka kwa inu.
עוד

ספרים הקשורים לכותר זה

The New Life Mission

השתתף בסקר שלנו

איך שמעת עלינו?