Search

مفت چپھیاں ھوئیاں کتاباں،
برقی کتاباں تے بولیاں ھوئیاں کتاباں

پانی تے رُوح دی خوشخبری

چیچھیوا 65

KODI CHOFUNIKIRA NDI CHIANI KWA INU KUTI MUBADWENSO MWATSOPANO?

Rev. Paul C. Jong | ISBN 9788928240876 | ورقے 397

ڈاؤن لوڈ کرو مفت ای-کتاباں تے آڈیو کتاباں

اپنی پسندیدہ فائل فارمیٹ چنو تے اپنے موبائل ڈیوائس، پی سی یا ٹیبلٹ تے محفوظ طریقے نال ڈاؤن لوڈ کرو تاں جو تسیں کدے وی، کتھے وی وعظاں دا مجموعہ پڑھ تے سن سکو۔ ساریاں ای-کتاباں تے آڈیو کتاباں بلکل مفت نیں۔

🔻تسیں تھلے دتے گئے پلیئر راہیں آڈیو کتاب سن سکدے او۔
پرنٹڈ کتاب دے مالک بنو
ایمیزون تے پرنٹڈ کتاب خریدو
Zamkatimu

Mawu Oyamba 
1. Kodi Ndindani Olambira Mumzimu Ndi M’coonadi? (Yohane 4:1-24) 
2. Kodi Zikutanthauza Chiani Kubadwadi Mwatsopano? (Yohane 4:1-19) 
3. Kanani Maganizo Anu (2 Mafumu 5:15-19)
4. Umunthu Wanu Weni Weni Ndi Chikondi Cha Ambuye (Yohane 3:16) 
5. Tiyenera Kubadwa Mwatsopano Pokhulupilira mu Uthenga Wabwino wa Madzi Ndi Mzimu (Yohane 3:1-5)
6. Chikhulupiliro Chomwe Chimagonjetsa Dziko Lino (Yohane 15:1-9) 
7. Kukhulupilira mu Ntchito Ya Mulungu Ndi Kugwira Ntchito Ya Mulungu (Yohane 6:16-29) 
8. Yesu Watsuka Mapazi athu Monga M’mene Anatsukira Mapazi a Petro (Yohane 13:1-11) 
9. Ambuye Wathu Watidalitsa Ife Kuti Titsate Iye Ngakhale Tiri Ndi Zolakwa Zambiri (Yohane 21:15-19)
10. Chofunikira Chenicheni Pogawana Chiyanjano Mwa Kristu (1 Yohane 1-10) 
11. Kodi Zikutanthauza Chiani Pamene Baibulo Lanena Kuti Yense Wakukhala Mwa Mulungu Sachimwa? (1 Yohane 3:1-10) 
12. Kodi Mukufunitsitsadi Kuti Chikhulupiliro Chanu Chikhale Chofanana Monga Chikhulupiliro Cha Petro? (Mateyu 16:13-20) 
13 Chilungamo Cha Ambuye Ndi Chofunika Kotheratu Kwa Ife Amene Timachita Tchimo Nthawi Zonse (Mateyu 9:9-13) 
 
Akristu lero ayenera kusintha maganizo ao. Iwo ayenera kukhulupilira mu Uthenga Wabwino wa madzi ndi Mzimu woperekedwa ndi Mulungu monga chipulumutso chao cheni cheni. Tonse tiyenera kuthokoza Ambuye potipatsa ife Uthenga umenewu Wabwino wa madzi ndi Mzimu. Kodi m’malo mwake tinganene bwanji kuti ntchito ya Ambuye ya chipulumutso yomwe yaombola ife ku machimo onse a dziko kuti ndiyolakwika? Kudzera m’bukuli pa Uthenga Wabwino wa madzi ndi Mzimu, ali yense tsopano ayenera kubadwa mwatsopano pokhulupilira muchipulumutso chomwe Ambuye wakwaniritsa kamodzi kokha. Ngati simukutsimikizabe za izi, muyenera kachiwiri kusinkhasinkha mwakuya pa chilungamo cha Mulungu chomwe Ambuye wapereka kwa inu.
ھور

اِس عنوان سے متعلقہ کتابیں

The New Life Mission

ساڈے سروے وچ حصہ پاؤ

تہانوں ساڈے بارے کنج پتہ چلیا؟